@nyapedr they are saying roughly, no matter what critics they face and no matter what hurdles they wont give up praising and doing God's work and that God will fight their battles for them. Hope that helps.
Iiiiiii koma anyamata ndi asikana inu mmmmh mumandimaliza kwabasi ndipo ndizoona ambuye akutimenyela nkhondo, siku ndi siku.Tikuona even maiko akunja ano kuti koma Mulungu alinafe ndithu pamenepa ndiye ndikumva bwino kwabasi ndikukumbukila mwana wanga amayikonda nyimbo imeneyi. A Malawi tiyeni tisasiye kupemphera. Ndakusowa mwana wanga zidalisika basi ndi Ndirande Anglican.
Beautiful country, beautiful people, great talent! Osamusiya ambuye!!! I love Malawi, the Warm Heart of Africa, surely supplying blood to the entire Africa.
I have been looking for this song for along time......next time try to put the song title alongside the singers. Bravo guys!!! Nyimbo ngati izi zimatikumbutsa ku mudzi ndithu!!!!!!!
This is surely a blessing not only when you are in far away lands but all the time! I hope the spirit of posting our local songs on the e-media won't be extinguished. Wawa a jorikk. Ife tonse omwe tili ndi mwayi wokhala ndi nyimbo zathuzi in video tiyeni tizigawana.
this song brought tears to my eyes even though I never understood a single word.
Yigabk 1 month ago
love this song pliz can anyone translate dont understand some words
nyapedr 6 months ago
@nyapedr they are saying roughly, no matter what critics they face and no matter what hurdles they wont give up praising and doing God's work and that God will fight their battles for them. Hope that helps.
sambukatha2 4 months ago
Amen to that..this is very beautiful i lk it i can listern to this song for the whole day.
guys u r really doing a great job keep it up...and God bless u all.
cytaable 9 months ago
Oh......Praise be to our Almighty God, this is a beautiful song, nice message
I remember listening to it when I was in lusaka zambia, then in lilongwe.
God bless this great choir......
Princejayize 1 year ago
Iiiiiii koma anyamata ndi asikana inu mmmmh mumandimaliza kwabasi ndipo ndizoona ambuye akutimenyela nkhondo, siku ndi siku.Tikuona even maiko akunja ano kuti koma Mulungu alinafe ndithu pamenepa ndiye ndikumva bwino kwabasi ndikukumbukila mwana wanga amayikonda nyimbo imeneyi. A Malawi tiyeni tisasiye kupemphera. Ndakusowa mwana wanga zidalisika basi ndi Ndirande Anglican.
MsTaque 1 year ago
God bless the Anglican church!
churchlad 2 years ago
thanks alot anyamata ndi asungwana potitsitsimutsa, groly be to the Lord!
rtaibu 2 years ago
hie Enelaw! his name is Denis, he`s blessed with the great voice.
chideza 2 years ago
ooh thnks menn..
Enelaw 2 years ago
Beautiful country, beautiful people, great talent! Osamusiya ambuye!!! I love Malawi, the Warm Heart of Africa, surely supplying blood to the entire Africa.
nganya1975 2 years ago
Osanamizana mukuimba bwino kwambiri nyimbo zosangalatsa. Ambuye akudaritseni. But what about New Lilongwe or New Jerusalem CCAP CHOIR?
chideza 2 years ago
Wow this is really Great, does anyone know the name of the Guy starting the song? He is so blessed and everyone else.
Enelaw 2 years ago
I have been looking for this song for along time......next time try to put the song title alongside the singers. Bravo guys!!! Nyimbo ngati izi zimatikumbutsa ku mudzi ndithu!!!!!!!
Mthyolamiti 2 years ago
koma nyimbo imeneyi yabwino bwanji
elizabethmbale 2 years ago
This is surely a blessing not only when you are in far away lands but all the time! I hope the spirit of posting our local songs on the e-media won't be extinguished. Wawa a jorikk. Ife tonse omwe tili ndi mwayi wokhala ndi nyimbo zathuzi in video tiyeni tizigawana.
emjimapemba 3 years ago
A lemekezeke Mulungu
sibongile909 3 years ago
zikomo
congomalawian 3 years ago
mwatidalitsa kwambili tikuthoza kwabasi mr. jorikk.
kenkasm2 3 years ago
I love this song...I remember the first time I heard it last year back home
CrazybutSane88 3 years ago